Yohane 1:17 - Buku Lopatulika17 Chifukwa chilamulo chinapatsidwa mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinadza mwa Yesu Khristu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Chifukwa chilamulo chinapatsidwa mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinadza mwa Yesu Khristu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Paja Mulungu adatipatsa Malamulo ake kudzera mwa Mose, koma kudzera mwa Yesu Khristu adatizindikiritsa kukoma mtima ndi kukhulupirika kwake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Pakuti lamulo linapatsidwa kudzera mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinabwera kudzera mwa Yesu Khristu. Onani mutuwo |