Yohane 1:16 - Buku Lopatulika16 Chifukwa mwa kudzala kwake tinalandira ife tonse, chisomo chosinthana ndi chisomo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chifukwa mwa kudzala kwake tinalandira ife tonse, chisomo chosinthana ndi chisomo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Kuchokera m'kukoma mtima kwake kwathunthu ife tonse tidalandira madalitso, madalitso ake otsatanatsatana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Kuchokera mʼkuchuluka kwa chisomo chake ife tonse talandira madalitso pamwamba pa madalitso. Onani mutuwo |