Yohane 1:18 - Buku Lopatulika18 Kulibe munthu anaona Mulungu nthawi zonse; Mwana wobadwa yekha wakukhala pa chifuwa cha Atate, Iyeyu anafotokozera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Kulibe munthu anaona Mulungu nthawi zonse; Mwana wobadwa yekha wakukhala pa chifuwa cha Atate, Iyeyu anafotokozera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Chikhalire palibe munthu amene adaona Mulungu, koma Mwana mmodzi yekha uja, amene ali wapamtima wa Atate, ndiye adaulula za Mulunguyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Palibe munthu amene anaona Mulungu, koma Mwana mmodzi yekhayo amene ali wa pamtima pa Atate, ndiye anafotokoza za Iye. Onani mutuwo |