Yeremiya 9:9 - Buku Lopatulika9 Kodi sindidzawalanga chifukwa cha izi? Ati Yehova; kodi moyo wanga sudzabwezera chilango mtundu wotere? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Kodi sindidzawalanga chifukwa cha izi? Ati Yehova; kodi moyo wanga sudzabwezera chilango mtundu wotere? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Kodi zimenezi ndipanda kuŵalanga nazo? Monga ndisaulipsire mtundu wotere wa anthu?” Akutero Chauta Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Kodi ndilekerenji kuwalanga chifukwa cha zimenezi? akutero Yehova. ‘Kodi ndisawulipsire mtundu wotere wa anthu?’ ” Onani mutuwo |