Yeremiya 9:10 - Buku Lopatulika10 Chifukwa cha mapiri ndidzagwa misozi ndi kulira, chifukwa cha mabusa a chipululu ndidzachita maliro, chifukwa apserera, kuti anthu sangathe kupitirirapo; ndiponso anthu sangathe kumva mau a ng'ombe zao; mbalame za mlengalenga ndi nyama zathawa, zapita. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Chifukwa cha mapiri ndidzagwa misozi ndi kulira, chifukwa cha mabusa a chipululu ndidzachita maliro, chifukwa apserera, kuti anthu sangathe kupitirirapo; ndiponso anthu sangathe kumva mau a ng'ombe zao; mbalame za mlengalenga ndi nyama zathawa, zapita. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ine ndidati, “Ndidzamva chisoni ndi kulira mokweza chifukwa cha mapiri. Ndidzadandaula chifukwa cha mabusa am'chipululu popeza kuti malo onsewo aonongeka. Palibe amene amapitako, sikumveka nkulira kwa ng'ombe komwe. Mbalame zonse zouluka ndiponso nyama zakuthengo zathaŵa, osaonekanso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Ndidzakhetsa misozi ndi kulira kwamphamvu chifukwa cha mapiri ndipo ndidzadandaula chifukwa cha msipu wa ku chipululu. Malo onsewo awonongeka ndipo palibe amene amapitako, ndipo sikumveka kulira kwa ngʼombe. Mbalame zamlengalenga zathawa ndipo nyama zakuthengo zachokako. Onani mutuwo |