Yeremiya 9:7 - Buku Lopatulika7 Chifukwa chake atero Yehova wa makamu, Taonani, ndidzawasungunula, ndi kuwayesa, pakuti ndidzachitanji, chifukwa cha mwana wamkazi wa anthu anga? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Chifukwa chake atero Yehova wa makamu, Taonani, ndidzawasungunula, ndi kuwayesa, pakuti ndidzachitanji, chifukwa cha mwana wamkazi wa anthu anga? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Nchifukwa chake Chauta Wamphamvuzonse akunena kuti, “Ndithu, anthu angaŵa ndidzaŵasungunula ngati chitsulo, ndipo ndidzaŵayesa. Iwowo ndi ochimwa, ndingathe bwanji kuŵalekerera? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Nʼchifukwa chake Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Taonani, Ine ndidzawasungunula ngati chitsulo ndi kuwayesa. Kodi ndingachite nawonso bwanji chifukwa cha machimo awo? Onani mutuwo |