Yeremiya 9:6 - Buku Lopatulika6 Ukhala pakati pa manyengo m'manyengo; akana kundidziwa, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ukhala pakati pa manyengo m'manyengo; akana kundidziwa, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Amasanjikiza tchimo pa tchimo linzake, chinyengo pa chinyengo chinzake. Amakana kundidziŵa,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Iwe wakhalira mʼchinyengo ndipo ukukana kundidziwa Ine,” akutero Yehova. Onani mutuwo |