Yeremiya 9:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo yense adzanyenga mnansi wake, osanena choonadi; aphunzitsa lilime lao kunena zonama; nadzithodwetsa kuchita zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo yense adzanyenga mnansi wake, osanena choonadi; aphunzitsa lilime lao kunena zonama; nadzithodwetsa kuchita zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Aliyense amanyenga mnzake, ndipo sanena zoona. Pakamwa pao adapazoloŵeza kulankhula zonama. Amakonda zoipa kwambiri, kotero kuti sangathenso kulapa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Aliyense amamunamiza mʼbale wake ndipo palibe amene amayankhula choonadi. Anapazoloweza pakamwa pawo kunena zabodza; amalimbika kuchita machimo. Onani mutuwo |