Yeremiya 8:9 - Buku Lopatulika9 Anzeru ali ndi manyazi, athedwa nzeru nagwidwa; taonani, akana mau a Yehova; ali nayo nzeru yotani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Anzeru ali ndi manyazi, athedwa nzeru nagwidwa; taonani, akana mau a Yehova; ali nayo nzeru yotani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Anthu anzeru adzachita manyazi, adzatha nzeru, ndipo adzagwidwa. Akana mau a Chauta, nanga nzeru zao nzotani? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Anthu anzeru achita manyazi; athedwa nzeru ndipo agwidwa. Iwo anakana mawu a Yehova. Nanga tsono nzeru zawo ziwapinduliranji? Onani mutuwo |