Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 8:8 - Buku Lopatulika

8 Bwanji muti, Tili ndi nzeru ife, ndi malamulo a Yehova ali ndi ife? Koma, taona, peni lonyenga la alembi lachita zonyenga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Bwanji muti, Tili ndi nzeru ife, ndi malamulo a Yehova ali ndi ife? Koma, taona, peni lonyenga la alembi lachita zonyenga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 “Mungathe kunena bwanji kuti, ‘Ndife anzeru, timasunga malamulo a Chauta, pamene alembi akulemba zabodza?’

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 “ ‘Inu mukunena bwanji kuti, ‘Ndife anzeru ndipo timasunga malamulo a Yehova?’ Koma ndi alembi anu amene akulemba zabodza.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 8:8
18 Mawu Ofanana  

Koma munthu wopanda pake asowa nzeru, ngakhale munthu abadwa ngati mwanawabulu.


Amchotsera wokhulupirika kunena kwake. Nalanda luntha la akulu.


Aonetsa mau ake kwa Yakobo; malemba ake, ndi maweruzo ake kwa Israele.


Zidzukulu ndizo korona wa okalamba; ndipo ulemerero wa ana ndiwo atate ao.


Atate wako woyamba anachimwa, ndi otanthauzira ako andilakwira Ine.


Ndipo iwo anati, Tiyeni, tilingalire Yeremiya chomchitira choipa; pakuti chilamulo sichidzathera wansembe, kapena uphungu wanzeru, kapena mau mneneri. Tiyeni, timpande iye ndi lilime, tisamvere iye mau ake ali onse.


Ndipo ndidzataya uphungu wa Yuda ndi wa Yerusalemu m'malo ano; ndipo ndidzagwetsa iwo ndi lupanga pamaso pa adani ao, ndi padzanja la iwo amene afuna moyo wao; mitembo yao ndidzapatsa ikhale chakudya cha mbalame za m'mlengalenga, ndi cha zilombo za dziko lapansi.


Ansembe sanati, Ali kuti Yehova? Ndi iwo amene agwira malamulo sandidziwa Ine; ndi abusa omwe anandilakwira Ine, ndi aneneri ananenera mwa Baala, natsata zinthu zosapindula.


Pakuti anthu anga apusa, sandidziwa Ine; ali ana opulukira sazindikira; ali ochenjera kuchita choipa koma kuchita chabwino sakudziwa.


Muti bwanji, Tili amphamvu, olimba mtima ankhondo?


Ndinamlembera zinthu zambirimbirizo za chilamulo changa, koma zinayesedwa ngati chinthu chachilendo.


iyeyo sadzalemekeza atate wake. Ndipo inu mupeputsa mau a Mulungu chifukwa cha miyambo yanu.


Yesu anati kwa iwo, Mukadakhala osaona simukadakhala nalo tchimo; koma tsopano munena, kuti, Tipenya: tchimo lanu likhala.


Pakunena kuti ali anzeru, anapusa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa