Yeremiya 8:5 - Buku Lopatulika5 Bwanji abwerera anthu awa a Yerusalemu chibwererere? Agwiritsa chinyengo, akana kubwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Bwanji abwerera anthu awa a Yerusalemu chibwererere? Agwiritsa chinyengo, akana kubwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chifukwa chiyani nanga anthu ameneŵa akupitirirabe kulakwa, osabwereranso? Akangamira ndithu machimo ao, akukana kubwerera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chifukwa chiyani nanga anthu awa akupitirirabe kuchimwa, osabwerera? Chifukwa chiyani Yerusalemu akubwerera mʼmbuyo? Iwo akangamira chinyengo; akukana kubwerera. Onani mutuwo |