Yeremiya 8:4 - Buku Lopatulika4 Ndiponso udzati kwa iwo, Atero Yehova, Kodi adzagwa, osaukanso? Kodi wina adzachoka, osabweranso? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndiponso udzati kwa iwo, Atero Yehova, Kodi adzagwa, osaukanso? Kodi wina adzachoka, osabweranso? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chauta adandiwuza kuti ndifunse anthu ake mau aŵa: “Kodi anthu akagwa, ndiye kuti sangathe kudzukanso? Kodi munthu akasokera, ndiye kuti sangathe kubwereranso? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “Tsono awuze anthuwa, ‘Yehova akuti: “ ‘Kodi anthu akagwa sangadzukenso? Munthu akasochera kodi sangathe kubwereranso? Onani mutuwo |