Yeremiya 8:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo otsala onse amene akutsala pa banja loipa ili adzasankha imfa koposa moyo, ndiwo amene atsala m'malo monse m'mene ndinawaingiramo, ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo otsala onse amene akutsala pa banja loipa ili adzasankha imfa koposa moyo, ndiwo amene atsala m'malo monse m'mene ndinawaingiramo, ati Yehova wa makamu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Anthu onse otsala mwa anthu a mtundu woipawu, kulikonse kumene ndaŵapirikitsira, adzakonda kufa kupambana kuti akhale ndi moyo,” akuterotu Chauta Wamphamvuzonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Otsala onse a mtundu woyipawu adzafuna imfa kopambana moyo kulikonse kumene ndidzawapirikitsirako, akutero Yehova Wamphamvuzonse.’ ” Onani mutuwo |