Yeremiya 7:16 - Buku Lopatulika16 Chifukwa chake iwe usapempherere anthu awa, usawakwezere iwo mfuu kapena pemphero, usandipembedze; pakuti Ine sindidzakumvera iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Chifukwa chake iwe usapempherere anthu awa, usawakwezere iwo mfuu kapena pemphero, usandipembedze; pakuti Ine sindidzakumvera iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 “Iwe Yeremiya, usaŵapempherere anthu ameneŵa. Usaŵapepesere kwa Ine kapena kuŵadandaulira mondiwumiriza chifukwa Ine sindikumvera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “Choncho iwe Yeremiya usawapempherere anthu awa ngakhale kuwapepesera kapenanso kuwapembedzera; usandidandaulire, chifukwa Ine sindidzakumvera. Onani mutuwo |