Yeremiya 7:17 - Buku Lopatulika17 Kodi suona iwe chimene achichita m'mizinda ya Yuda ndi m'miseu ya Yerusalemu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Kodi suona iwe chimene achichita m'midzi ya Yuda ndi m'miseu ya Yerusalemu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Kodi sukuwona zimene zikuchitika m'mizinda ya ku Yuda ndi m'miseu ya m'Yerusalemu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kodi sukuona zimene akuchita mʼmizinda ya ku Yuda ndi mʼmisewu ya ku Yerusalemu? Onani mutuwo |
Koma tidzachita ndithu mau onse anatuluka m'kamwa mwathu, kufukizira mfumu yaikazi ya kumwamba, ndi kumthirira iye nsembe zothira, monga momwe tinkachitira ife, ndi atate athu, ndi mafumu athu ndi akulu athu, m'mizinda ya Yuda, ndi m'miseu ya Yerusalemu, pakuti pamenepo tinali ndi chakudya chokwanira, tinakhala bwino, sitinaona choipa.