Yeremiya 7:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo ndidzakuchotsani inu pamaso panga, monga ndinachotsa abale anu onse, mbeu zonse za Efuremu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo ndidzakuchotsani inu pamaso panga, monga ndinachotsa abale anu onse, mbeu zonse za Efuremu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndidzakuchotsani pamaso panga monga momwe ndidachotsera abale anu onse, zidzukulu zonse za Efuremu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Ndidzakuthamangitsani pamaso panga, ngati momwe ndinachitira abale anu onse, anthu a Efereimu.’ ” Onani mutuwo |