Yeremiya 6:7 - Buku Lopatulika7 Monga kasupe atulutsa madzi ake, chomwecho atulutsa zoipa zake; chiwawa ndi kufunkha zimveka m'kati mwake; pamaso panga masiku onse pali kulira ndi mabala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Monga kasupe atulutsa madzi ake, chomwecho atulutsa zoipa zake; chiwawa ndi kufunkha zimveka m'kati mwake; pamaso panga masiku onse pali kulira ndi mabala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Monga momwe chitsime chimasungira madzi ake, ndimonso m'mene mzindawo umasungira zoipa zake. Zimene mukumva ndi za chiwonongeko ndi za nkhondo. Ndikuwonamonso matenda ndi zilonda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Monga momwe chitsime chimatulutsira madzi ndi mmenenso Yerusalemu amatulutsira zoyipa zake. Chiwawa ndi chiwonongeko ndi zomwe zimamveka mu mzindamo; nthenda yake ndi mabala ake ndimaziona nthawi zonse. Onani mutuwo |