Yeremiya 6:8 - Buku Lopatulika8 Ulangizidwe, Yerusalemu, ungakuchokere moyo wanga, ndingakuyese iwe bwinja, dziko losakhalamo anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ulangizidwe, Yerusalemu, ungakuchokere moyo wanga, ndingakuyese iwe bwinja, dziko losakhalamo anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Iwe Yerusalemu, tengapo phunziro, kuwopa kuti chikondi changa pa iwe chingathe, ndipo ndingakusandutse dziko lachipululu, dziko lopanda anthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iwe Yerusalemu, tengapo phunziro, kuopa kuti chikondi changa pa iwe chingakuchokere ndi kusandutsa dziko lako kukhala bwinja mopanda munthu wokhalamo.” Onani mutuwo |