Yeremiya 6:6 - Buku Lopatulika6 Pakuti Yehova wa makamu atero, Dulani mitengo, unjikani nthumbira pomenyana ndi Yerusalemu; mzinda wakudzalangidwa ndi uwu; m'kati mwake modzala nsautso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pakuti Yehova wa makamu atero, Dulani mitengo, unjikani nthumbira pomenyana ndi Yerusalemu; mudzi wakudzalangidwa ndi uwu; m'kati mwake modzala nsautso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mau a Chauta Wamphamvuzonse akuti, “Gwetsani mitengo ya mu Yerusalemu, ndipo mzindawu muumangire nthumbira zankhondo. Mzinda umenewu ndi woyenera kulangidwa, anthu ake amangokhalira kuzunzana. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Dulani mitengo ndipo mumange mitumbira yankhondo kulimbana ndi Yerusalemu. Mzinda umenewu uyenera kulangidwa; wadzaza ndi kuponderezana. Onani mutuwo |