Yeremiya 6:2 - Buku Lopatulika2 Ndidzachotsa mwana wamkazi wa Ziyoni mkazi wokoma ndi wololopoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndidzachotsa mwana wamkazi wa Ziyoni mkazi wokoma ndi wololopoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndidzauwononga mzinda wa Ziyoni, mzinda wooneka bwino ndi wokongola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Kodi mzinda wa Ziyoni suli ngati msipu wokongola kwambiri, kumene abusa amafikako ndi ziweto zawo? Onani mutuwo |