Yeremiya 6:3 - Buku Lopatulika3 Abusa ndi nkhosa zao adzadza kwa iye; adzamanga mahema ao pomzinga iye; adzadya yense pokhala pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Abusa ndi nkhosa zao adzadza kwa iye; adzamanga mahema ao pomzinga iye; adzadya yense pokhala pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Mafumu adzabwera ndi asilikali ao. Adzamanga zithando momzinga Yerusalemu, ndipo aliyense adzakhazika anthu ake pamalo pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Abusa ndi nkhosa zawo adzabwera kudzalimbana nawo; adzamanga matenti awo mowuzinga, ndipo aliyense adzakhazika anthu ake pamalo pake.” Onani mutuwo |