Yeremiya 51:9 - Buku Lopatulika9 Tikadachiritsa Babiloni koma sanachire; mumsiye iye, tipite tonse yense kudziko lake; pakuti chiweruziro chake chifikira kumwamba, chinyamulidwa mpaka kuthambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Tikadachiritsa Babiloni koma sanachire; mumsiye iye, tipite tonse yense kudziko lake; pakuti chiweruziro chake chifikira kumwamba, chinyamulidwa mpaka kuthambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ena adati, ‘Tidayesa kumpatsa mankhwala koma sadachire. Tiyeni tingomsiya, timchokere ndipo aliyense apite ku dziko lakwao. Paja mlandu wake wafika mpaka kumwamba, wafika mpaka ku mlengalenga.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ena anati, “ ‘Ife tinayesa kumupatsa mankhwala Babuloni, koma sanachire; tiyeni timusiye ndipo aliyense apite ku dziko la kwawo, pakuti mlandu wake wafika mpaka mlengalenga, wafika mpaka kumwamba.’ Onani mutuwo |