Yeremiya 51:8 - Buku Lopatulika8 Babiloni wagwa dzidzidzi naonongedwa; mumkuwire iye; mutengere zowawa zake vunguti, kapena angachire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Babiloni wagwa dzidzidzi naonongedwa; mumkuwire iye; mutengere zowawa zake vunguti, kapena angachire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Babiloni wagwa mwadzidzidzi ndipo waonongeka. Mlireni, mfunireni mankhwala, kuti mwina nkuchira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Babuloni wagwa mwadzidzidzi ndi kusweka. Mulireni! Mfunireni mankhwala opha ululu wake; mwina iye nʼkuchira.” Onani mutuwo |