Yeremiya 5:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo ngakhale ati, Pali Yehova; komatu alumbira monama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo ngakhale ati, Pali Yehova; komatu alumbira monama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ngakhale anthu akulumbira m'dzina la Chauta wamoyo, komabe akungolumbira monama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ngakhale anthu akulumbira kuti, ‘Pali Yehova wamoyo,’ komabe akungolumbira mwachinyengo.” Onani mutuwo |