Yeremiya 5:1 - Buku Lopatulika1 Thamangani inu kwina ndi kwina m'miseu ya Yerusalemu, taonanitu, dziwani, ndi kufunafuna m'mabwalo ake, kapena mukapeza munthu, kapena alipo wakuchita zolungama, wakufuna choonadi; ndipo ndidzamkhululukira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Thamangani inu kwina ndi kwina m'miseu ya Yerusalemu, taonanitu, dziwani, ndi kufunafuna m'mabwalo ake, kapena mukapeza munthu, kapena alipo wakuchita zolungama, wakufuna choonadi; ndipo ndidzamkhululukira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Thamangani uku ndi uku m'miseu ya Yerusalemu, mudziwonere nokha. Funafunani ku mabwalo ake ngati mungapezeke munthu, munthu wake wochita zolungama, wofunitsitsa zoona, kuti choncho Yerusalemu ndidzamkhululukire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Pitani uku ndi uku mʼmisewu ya Yerusalemu, mudzionere nokha, funafunani mʼmabwalo ake. Ngati mungapeze munthu mmodzi amene amachita zachilungamo ndi kufunafuna choonadi, ndipo ndidzakhululukira mzinda uno. Onani mutuwo |