Yeremiya 5:18 - Buku Lopatulika18 Koma masiku onsewo, ati Yehova, sindidzatsirizitsa konse ndi iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma masiku onsewo, ati Yehova, sindidzatsirizitsa konse ndi iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 “Koma ngakhale pa masiku amenewo sindidzakuwonongani kotheratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “Komabe pa masiku amenewo sindidzakuwonongani kotheratu,” akutero Yehova. Onani mutuwo |