Yeremiya 5:17 - Buku Lopatulika17 Adzadya zokolola zako, ndi mkate wako, umene ana ako aamuna ndi aakazi ayenera kudya; adzadya nkhosa zako ndi zoweta zako; adzadya mphesa zako ndi nkhuyu zako; adzapasula ndi lupanga mizinda yamalinga yako, imene ukhulupiriramo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Adzadya zokolola zako, ndi mkate wako, umene ana ako aamuna ndi aakazi ayenera kudya; adzadya nkhosa zako ndi zoweta zako; adzadya mphesa zako ndi nkhuyu zako; adzapasula ndi lupanga midzi yamalinga yako, imene ukhulupiriramo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Adzakutherani zokolola zanu ndi chakudya chanu. Adzapha ana anu aamuna ndi aakazi, adzakupheraninso nkhosa zanu ndi ng'ombe zanu. Adzaononga mipesa yanu ndi mikuyu yanu. Adzagwetsa mwankhondo mizinda yanu yamalinga imene mumaidalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Adzakudyerani zokolola zanu ndi chakudya chanu, adzapha ana anu aamuna ndi aakazi; adzakupherani nkhosa zanu ndi ngʼombe zanu, adzawononga mpesa wanu ndi mikuyu yanu. Ndi malupanga awo adzagwetsa mizinda yanu yotetezedwa imene mumayidalira. Onani mutuwo |