Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 5:16 - Buku Lopatulika

16 Phodo lao lili ngati manda apululu, onsewo ndiwo olimba.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Phodo lao lili ngati manda apululu, onsewo ndiwo olimba.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Ankhondowo mipaliro yao imapha anthu ambirimbiri, onsewo ndi ngwazi zokhazokha pa nkhondo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Zida zawo za nkhondo zapha anthu ambirimbiri; onsewo ndi ankhondo amphamvu okhaokha.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 5:16
7 Mawu Ofanana  

Pakuti m'kamwa mwao mulibe mau okhazikika; m'kati mwao m'mosakaza; m'mero mwao ndi manda apululu; lilime lao asyasyalika nalo.


Mauta ao adzatha anyamata; ndipo sadzachitira chisoni chipatso cha mimba; diso lao silidzaleka ana.


amene mivi yao ili yakuthwa, ndi mauta ao onse athifuka; ziboda za akavalo ao zidzayesedwa ngati mwala, ndi njinga zao ngati kamvulumvulu;


Yehova atero, Taona, mtundu wa anthu uchokera kumpoto; ndi mtundu waukulu udzaukitsidwa ku malekezero a dziko lapansi.


Agwira uta ndi nthungo; ali ankharwe, alibe chifundo; mau ao apokosera ngati nyanja, akwera pa akavalo; aguba monga anthu ofuna kumenyana nkhondo ndi iwe, mwana wamkazi wa Ziyoni.


Walasa impso zanga ndi mivi ya m'phodo mwake.


M'mero mwao muli manda apululu; ndi lilime lao amanyenga; ululu wa mamba uli pansi pa milomo yao;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa