Yeremiya 5:16 - Buku Lopatulika16 Phodo lao lili ngati manda apululu, onsewo ndiwo olimba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Phodo lao lili ngati manda apululu, onsewo ndiwo olimba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ankhondowo mipaliro yao imapha anthu ambirimbiri, onsewo ndi ngwazi zokhazokha pa nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Zida zawo za nkhondo zapha anthu ambirimbiri; onsewo ndi ankhondo amphamvu okhaokha. Onani mutuwo |