Yeremiya 5:12 - Buku Lopatulika12 Akana Yehova, ndi kuti, Si ndiye; choipa sichidzatifika ife; sitidzaona kapena lupanga kapena njala; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Akana Yehova, ndi kuti, Si ndiye; choipa sichidzatifika ife; sitidzaona kapena lupanga kapena njala; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Anthuwo ankanama ponena za Chauta, ankati, “Mulungu sangatichite kanthu. Choipa sichidzatigwera, sitidzaona nkhondo kapena njala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Iwowa ankanama ponena za Yehova kuti, “Yehova sangachite zimenezi! Choyipa sichidzatigwera; sitidzaona nkhondo kapena njala. Onani mutuwo |