Yeremiya 5:11 - Buku Lopatulika11 Pakuti nyumba ya Israele ndi nyumba ya Yuda zinandichitira monyenga kwambiri, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Pakuti nyumba ya Israele ndi nyumba ya Yuda zinandichitira monyenga kwambiri, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Anthu a ku Israele ndi a ku Yuda onse akhala osakhulupirika kwa Ine,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Nyumba ya Israeli ndi nyumba ya Yuda onse akhala osakhulupirika kotheratu kwa Ine.” Onani mutuwo |