Yeremiya 5:10 - Buku Lopatulika10 Kwerani pa makoma ake nimupasule; koma musatsirize konse; chotsani nthambi zake pakuti sizili za Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Kwerani pa makoma ake nimupasule; koma musatsirize konse; chotsani nthambi zake pakuti sizili za Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono ndidzatuma adani kuti akaononge mizere ya mipesa yao, komabe osati kotheratu. Akasadze nthambi zake, poti anthu ameneŵa si ake a Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 “Pitani ku minda yake ya mipesa ndi kukayiwononga, koma musakayiwononge kotheratu. Sadzani nthambi zake pakuti anthu amenewa si a Yehova. Onani mutuwo |
taonani, Ine, ndidzatuma ndi kutenga mabanja onse a kumpoto, ati Yehova, ndipo ndidzatuma kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni, mtumiki wanga, ndipo ndidzatengera iwo padziko lino, ndi pa okhalamo ake onse, ndi pa mitundu iyi yozungulira, ndipo ndidzathetsa iwo ndithu, ndi kuwayesa iwo chizizwitso, ndi chotsonyetsa, ndi bwinja lamuyaya.