Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 48:5 - Buku Lopatulika

5 Pakuti adzakwera pa chikweza cha Luhiti ndi kulira kosaleka; pakuti pa chitsiko cha Horonaimu amva kulira kowawa kwa chionongeko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Pakuti adzakwera pa chikweza cha Luhiti ndi kulira kosaleka; pakuti pa chitsiko cha Horonaimu amva kulira kowawa kwa chionongeko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Anthu akupita nalira kwambiri pa chikwera cha ku Luhiti. Kulira kwa chiwonongeko kukumveka ku matsitso a ku Horonaimu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Anthu akukwera chikweza cha ku Luhiti, akulira kwambiri pamene akupita. Kulira chifukwa cha chiwonongeko kukumveka pa njira yotsikira ku Horonaimu.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 48:5
3 Mawu Ofanana  

Mtima wanga ufuula chifukwa cha Mowabu: akulu ake athawira ku Zowari, ku Egilati-Selisiya; pakuti pa chikweza cha Luhiti akwera alikulira, pakuti m'njira ya Horonaimu akweza mfuu wa chionongeko.


Mau amveka kuchokera ku Horonaimu, kufunkha ndi kuononga kwakukulu!


Mowabu waonongedwa; ang'ono ake amveketsa kulira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa