Yeremiya 48:4 - Buku Lopatulika4 Mowabu waonongedwa; ang'ono ake amveketsa kulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mowabu waonongedwa; ang'ono ake amveketsa kulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mowabu waonongeka, ana ake akulira kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mowabu wawonongeka; ana ake angʼonoangʼono akulira kwambiri. Onani mutuwo |