Yeremiya 48:3 - Buku Lopatulika3 Mau amveka kuchokera ku Horonaimu, kufunkha ndi kuononga kwakukulu! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Mau amveka kuchokera ku Horonaimu, kufunkha ndi kuononga kwakukulu! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 “Imvani kulira kwachisoni kwa anthu a ku Horonaimu, akuti, ‘Chisakazo ndi chiwonongeko chachikulutu!’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Tamvani mfuwu wa anthu a ku Horonaimu. Iwo akulira kuti, ‘Kusakazika ndi kuwonongeka kwakukulu.’ Onani mutuwo |