Yeremiya 48:2 - Buku Lopatulika2 Palibenso kutamanda Mowabu; mu Hesiboni anamlingiririra zoipa, ndi kuti, Tiyeni, tiwathe asakhalenso mtundu wa anthu. Iwenso, Madimeni, udzatontholetsedwa, lupanga lidzakulondola iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Palibenso kutamanda Mowabu; m'Hesiboni anamlingiririra zoipa, ndi kuti, Tiyeni, tiwathe asakhalenso mtundu wa anthu. Iwenso, Madimeni, udzatontholetsedwa, lupanga lidzakulondola iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mowabu sakutchukanso. Adampanganirana zachiwembu ku Hesiboni, adati, ‘Tiyeni timuwononge, asakhalenso mtundu wa anthu.’ Ndipo inu okhala ku Madimeni, adzakukhalitsani chete, adzakupirikitsani ndi lupanga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Palibenso amene akutamanda Mowabu; ku Hesiboni anthu anamupanganira zoyipa: ‘Bwerani, tiyeni timuwonongeretu kuti asakhalenso mtundu wa anthu.’ Inunso anthu a ku Madimena, adzakukhalitsani chete; ankhondo adzakupirikitsani. Onani mutuwo |