Yeremiya 48:1 - Buku Lopatulika1 Za Mowabu. Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Tsoka Nebo! Pakuti wapasuka; Kiriyataimu wachitidwa manyazi, wagwidwa; linga la pamtunda lachitidwa manyazi lapasudwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Za Mowabu. Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Tsoka Nebo! Pakuti wapasuka; Kiriyataimu wachitidwa manyazi, wagwidwa; linga la pamtunda lachitidwa manyazi lapasudwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ponena za Mowabu, Chauta Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israele, akuti, “Tsoka kwa mzinda wa Nebo, wasanduka chipululu. Kiriyataimu wachititsidwa manyazi, wagonjetsedwa. Linga lake lankhondo alinyoza ndipo aligumula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ponena za Mowabu: Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, “Tsoka kwa mzinda wa Nebo, chifukwa wawonongedwa. Mzinda wa Kiriyataimu wachititsidwa manyazi ndipo wagonjetsedwa; linga lichititsidwa manyazi ndipo lagumulidwa. Onani mutuwo |