Yeremiya 47:7 - Buku Lopatulika7 Udzakhala chete bwanji, popeza Yehova anakulangiza? Za Asikeloni, ndi za m'mphepete mwa nyanja, pamenepo analiika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Udzakhala chete bwanji, popeza Yehova anakulangiza? Za Asikeloni, ndi za m'mphepete mwa nyanja, pamenepo analiika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Kodi lupangalo lingapumule bwanji pamene Chauta walipatsa kale ntchito yoti limchitire? Walituma kuti likalimbane ndi Asikeloni, kuti likathire nkhondo anthu a m'mbali mwa nyanja.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma lupangalo lidzapumula bwanji pamene Yehova walilamulira kuti lithire nkhondo Asikeloni ndi anthu a mʼmbali mwa nyanja?” Onani mutuwo |