Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 45:2 - Buku Lopatulika

2 Yehova Mulungu wa Israele atero kwa inu, Baruki:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 Yehova Mulungu wa Israele atero kwa inu, Baruki:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 “Chauta, Mulungu wa Israele, akunena kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 “Yehova Mulungu wa Israeli, akunena kwa iwe Baruki kuti:

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 45:2
8 Mawu Ofanana  

M'mazunzo ao onse Iye anazunzidwa, ndipo mthenga wakuimirira pamaso pake anawapulumutsa; m'kukonda kwake ndi m'chisoni chake Iye anawaombola, nawabereka nawanyamula masiku onse akale.


Mau amene ananena Yeremiya mneneri kwa Baruki mwana wake wa Neriya, pamene analemba mau awa m'buku ponena Yeremiya, chaka chachinai cha Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, ndi kuti,


Munati, Kalanga ine tsopano! Pakuti Yehova waonjezera chisoni pa zowawa zanga; ndalema ndi kubuula kwanga, sindipeza kupuma.


Koma mukani, uzani ophunzira ake, ndi Petro, kuti akutsogolerani inu ku Galileya; kumeneko mudzamuona Iye, monga ananena ndi inu.


wotitonthoza ife m'nsautso yathu yonse, kuti tidzathe ife kutonthoza iwo okhala m'nsautso iliyonse, mwa chitonthozo chimene titonthozedwa nacho tokha ndi Mulungu.


Koma Iye amene atonthoza odzichepetsa, ndiye Mulungu, anatitonthoza ife ndi kufika kwake kwa Tito;


Pakuti popeza adamva zowawa, poyesedwa yekha, akhoza kuthandiza iwo amene ayesedwa.


Pakuti sitili naye mkulu wa ansembe wosatha kumva chifundo ndi zofooka zathu; koma wayesedwa m'zonse monga momwe ife, koma wopanda uchimo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa