Yeremiya 45:1 - Buku Lopatulika1 Mau amene ananena Yeremiya mneneri kwa Baruki mwana wake wa Neriya, pamene analemba mau awa m'buku ponena Yeremiya, chaka chachinai cha Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Mau amene ananena Yeremiya mneneri kwa Baruki mwana wake wa Neriya, pamene analemba mau awa m'buku ponena Yeremiya, chaka chachinai cha Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Naŵa mau amene mneneri Yeremiya adalembetsa Baruki mwana wa Neriya m'buku, chaka chachinai cha ufumu wa Yehoyakimu mwana wa Yosiya mfumu ya ku Yuda: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Uwu ndi uthenga umene mneneri Yeremiya anawuza Baruki mwana wa Neriya mʼchaka cha chinayi cha Yehoyakimu mwana wa mwana ya Yosiya kuti alembe mʼbuku. Onani mutuwo |