Yeremiya 41:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo panali, pamene analowa pakati pa mzinda, Ismaele mwana wa Netaniya anawapha, nawaponya pakati pa dzenje, iye ndi anthu okhala naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo panali, pamene analowa pakati pa mudzi, Ismaele mwana wa Netaniya anawapha, nawaponya pakati pa dzenje, iye ndi anthu okhala naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Atangofika pakati pa mudzi, Ismaele mwana wa Netaniya ndi anthu ake, adaŵapha onsewo naŵataya m'chitsime. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Atafika pakati pa mzinda, Ismaeli mwana wa Netaniya pamodzi ndi anthu amene anali naye anawapha anthuwo ndi kuwaponya mʼchitsime. Onani mutuwo |