Yeremiya 40:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo kapitao wa alonda anatenga Yeremiya, nati kwa iye, Yehova Mulungu wako ananenera choipa ichi malo ano; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo kapitao wa alonda anatenga Yeremiya, nati kwa iye, Yehova Mulungu wako ananenera choipa ichi malo ano; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mtsogoleriyo adatenga Yeremiya namuuza kuti, “Chauta, Mulungu wako, adanena kuti adzaononga malo ano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mtsogoleriyu anamupeza Yeremiya, anamuwuza kuti, “Yehova Mulungu wako analengeza kale zakuti malo ano adzawonongedwa. Onani mutuwo |