Yeremiya 4:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo udzalumbira, Pali Yehova m'zoonadi, m'chiweruziro, ndi m'chilungamo; ndipo mitundu ya anthu idzadzidalitsa mwa Iye, ndipo mwa Iye adzatamandira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo udzalumbira, Pali Yehova m'zoonadi, m'chiweruziro, ndi m'chilungamo; ndipo mitundu ya anthu idzadzidalitsa mwa Iye, ndipo mwa Iye adzatamandira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Muzilumbira moona kuti, ‘Pali Chauta wamoyo.’ Muzichita zimenezi mwachilungamo ndi mokhulupirika. Mukatero, anthu a mitundu yonse adzandipempha kuti ndiŵadalitse, ndipo adzanditamanda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Muzilumbira mokhulupirika ndiponso mwa chilungamo kuti, ‘Pali Yehova wamoyo.’ Mukatero anthu a mitundu ina yonse adzandipempha kuti ndiwadalitse ndipo adzanditamanda.” Onani mutuwo |