Yeremiya 4:1 - Buku Lopatulika1 Ngati udzabwera, Israele, ati Yehova, udzabwera kwa Ine; ndipo ngati udzachotsa zonyansa zako pamaso panga sudzachotsedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ngati udzabwera, Israele, ati Yehova, udzabwera kwa Ine; ndipo ngati udzachotsa zonyansa zako pamaso panga sudzachotsedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Ngati mukufuna kubwerera, inu Aisraele, bwererani kwa Ine,” akuterotu Chauta. “Chotsani mafano anu amene akundinyansaŵa, ndipo musasokerenso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Ngati mukufuna kubwerera, inu Aisraeli, bwererani kwa Ine,” akutero Yehova. “Chotsani mafano anu onyansa pamaso panga ndipo musasocherenso. Onani mutuwo |