Yeremiya 4:18 - Buku Lopatulika18 Njira yako ndi ntchito zako zinakuchitira izi; ichi ndicho choipa chako ndithu; chili chowawa ndithu, chifikira kumtima wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Njira yako ndi ntchito zako zinakuchitira izi; ichi ndicho choipa chako ndithu; chili chowawa ndithu, chifikira kumtima wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 “Zimenezi zakugwerani, inu Ayuda, chifukwa cha makhalidwe anu oipa ndi zochita zanu. Chimenechi ndiye chilango chanu, nchoŵaŵa kwambiri, chokalasa mpaka ku mtima.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “Makhalidwe anu ndi zochita zanu zakubweretserani zimenezi. Chimenechi ndiye chilango chanu. Nʼchowawa kwambiri! Nʼcholasa mpaka mu mtima!” Onani mutuwo |