Yeremiya 4:19 - Buku Lopatulika19 Matumbo anga, matumbo anga! Ndipoteka pamtima panga penipeni; mtima wanga sukhala pansi m'kati mwanga; sindithai kutonthola; pakuti wamva, moyo wanga, mau a lipenga, mbiri ya nkhondo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Matumbo anga, matumbo anga! Ndipoteka pamtima panga penipeni; mtima wanga sukhala pansi m'kati mwanga; sindithai kutonthola; pakuti wamva, moyo wanga, mau a lipenga, mbiri ya nkhondo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Mayo, mayo, ati kupweteka ati! Ha, mtima wanga ukuŵaŵa, ukugunda moti thithithi. Sindingathe kukhala chete. Ndikumva kulira kwa lipenga ndi mfuu yankhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mayo, mayo, ndikumva kupweteka! Aa, mtima wanga ukupweteka, ukugunda kuti thi, thi, thi. Sindingathe kukhala chete. Pakuti ndamva kulira kwa lipenga; ndamva mfuwu wankhondo. Onani mutuwo |