Yeremiya 4:17 - Buku Lopatulika17 Monga adindo a m'munda amzinga iye; chifukwa andipandukira Ine, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Monga adindo a m'munda amzinga iye; chifukwa andipandukira Ine, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Akuzinga Yerusalemu ngati alonda a munda, chifukwa choti anthu andipandukira,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Azinga Yerusalemu ngati anthu olondera munda, chifukwa Yerusalemu wandiwukira,’ ” akutero Yehova. Onani mutuwo |