Yeremiya 39:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo Nebuzaradani kapitao wa alonda anatenga anthu otsalira m'mzinda, ndi othawa omwe, opandukira, ndi kumtsata ndi anthu otsalira nanka nao am'nsinga ku Babiloni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo Nebuzaradani kapitao wa alonda anatenga anthu otsalira m'mudzi, ndi othawa omwe, opandukira, ndi kumtsata ndi anthu otsalira nanka nao am'nsinga ku Babiloni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Nebuzaradani, mtsogoleri wa alonda ankhondo, adatenga anthu onse otsala a mumzindawo kupita nawo ku Babiloni. Ameneŵa ndiwo amene adaadzipereka kwa iye, ndiponso anthu amene adaatsalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Nebuzaradani, mtsogoleri wa alonda ankhondo a mfumu, anatenga ukapolo anthu onse otsala mu mzindamo kupita nawo ku Babuloni, pamodzi ndi amene anadzipereka kale kwa iye. Onani mutuwo |