Yeremiya 39:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo Ababiloni anatentha ndi moto nyumba ya mfumu, ndi nyumba za anthu, nagumula malinga a Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo Ababiloni anatentha ndi moto nyumba ya mfumu, ndi nyumba za anthu, nagumula malinga a Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Ababiloni adatentha nyumba yaufumu, Nyumba ya Chauta pamodzi ndi nyumba zina zonse za anthu. Ndipo adagwetsa malinga a Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ababuloni anatentha nyumba ya mfumu ndi nyumba za anthu, ndiponso anagwetsa malinga a Yerusalemu. Onani mutuwo |