Yeremiya 3:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo kunali kuti mbiri ya dama lake inaipitsa dziko, ndipo anachita chigololo ndi miyala ndi mitengo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo kunali kuti mbiri ya dama lake inaipitsa dziko, ndipo anachita chigololo ndi miyala ndi mitengo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Dama la Israele linali lochititsa manyazi, kotero kuti potsiriza pake adaipitsa dziko. Adachita chigololo popembedza mafano amiyala ndi amitengo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Chiwerewere cha Israeli chinali chochititsa manyazi kotero kuti chinayipitsa dziko lonse. Anachita chigololo popembedza mafano a miyala ndi mitengo. Onani mutuwo |