Yeremiya 3:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo zingakhale zonsezi Yuda mphwake wonyenga sanabwere kwa Ine ndi mtima wake wonse, koma monama, ati Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo zingakhale zonsezi Yuda mphwake wonyenga sanabwere kwa Ine ndi mtima wake wonse, koma monama, ati Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Komabe atachita zonsezi, Yuda mbale wake wosakhulupirika uja sadabwerere kwa Ine ndi mtima wonse, koma mwachiphamaso chabe,” akuterotu Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Israeli atachita zonsezi, Yuda mʼbale wake wosakhulupirika uja sanabwerere kwa Ine ndi mtima wake wonse, koma mwachiphamaso chabe,” akutero Yehova. Onani mutuwo |